Pambuyo posintha pang'ono bolodi la zilengezo lomwe linali m'chipinda chathu chochezera, ndinapeza malo abwino kwambiri oti ndigawireko Kampeni ya Mawu a Chikondi cha Amayi!
Pa nthawi yopuma khofi kapena pamene ndikudya nkhomaliro, cholinga changa ndi kudziwitsa anzanga a kuntchito za Mawu a Chikondi cha Amayi.
Ndikukhulupirira kuti osati mimba zawo zokha zidzadzaza ndi kukhuta komanso mitima yawo idzakhutanso!
© Kutulutsa kapena kugawa kosaloledwa ndikoletsedwa.
27